Login to BlackFacts.com using your favorite Social Media Login. Click the appropriate button below and you will be redirected to your Social Media Website for confirmation and then back to Blackfacts.com once successful.
Enter the email address and password you used to join BlackFacts.com. If you cannot remember your login information, click the “Forgot Password” link to reset your password.
Mtsogoleri wakale wa dziko lino Dr Joyce Banda wanyamuka lero kupita mdziko la Kenya komwe watumidwa ndi a Lazarus Chakwera kukawaimilira pa maliro a mtsogoleri wakale wa dzikolo a Mwai Kibaki. A Kibaki omwe anali ndizaka 90, anamwalira lachinayi sabata yatha pa 21 April ndipo thupi lawo likuyembekezeka kulowa mmanda loweluka lino pa 30 April. […]
The post Chakwera atuma Joyce Banda ku maliro appeared first on Malawi 24.